The National AIDS Commission (NAC) and the Pharmacy and Medicines Regulatory Authority (PMRA), pursuant to their mandates under the HIV and AIDS (Prevention and Management) Act No. 9 of 2018 and the PMRA Act No. 9 of 2019, respectively, have noted with concern increased spread of false, inaccurate and misleading information on HIV treatment, often...
Day: July 11, 2024
Post
KUCHULUKA KWA NCHITIDWE OFALITSA MAUTHENGA ABODZA OKHUDZA MANKHWALA A HIV NDI EDZI MMASAMBA A MCHEZO
Mabungwe a National AIDS Commission (NAC) ndi Pharmacy and Medicines Regulatory Authority (PMRA) adapatsidwa mphamvu ndi malamulo yowunika ndi kuvomereza mauthenga okhudza matenda a edzi komanso kuwonetsetsa kuti mankhwala achipatala, mankhwala a zitsamba ndi zakudya kapena zakumwa zimene zili mgulu la mankhwala ndi zabwino, zotetezeka ndi zogwira ntchito bwino, komanso kuti malamulo okhudza ntchito za...