Unduna wa zaUmoyo ukudziwitsa anthu kuti ntchito yopeleka thandizo lolimbana ndi kachilombo ka HIV lipitilila muzipatala zonse za dziko lino .Undunawu ukudziwitsa anthu kuti tili ndi mankhwala a ARV ndi mankhwala ena onse olimbana ndi kachilombo ka HIV ndi matenda a Edzi okwanila m’dziko muno. Kuonjezera apo, undunawu ukuyembekezera kulandilaso mankhwala ena ndipo upitilila kudziwitsa...
Category: News
MINISTRY OF HEALTH PRESS RELEASE – ASSURANCE OF SUSTAINED DELIVERY OF HIV/AIDS SERVICES IN ALL PUBLIC AND PRIVATE HEALTH FACILITIES IN MALAWI
The Ministry of Health wishes to inform the public that all HIV/AIDS services will continue to be provided normally in all the public and private health facilities across the country.The Ministry, wishes to inform the public that the country has adequate quantities of ARVs, test kits and other supplies. Further, the Ministry has put measures...
Community Linkage Groups (CLGs) Gets A Timely Boost
It was all joy and jubilation in Lilongwe, Area 47 at Malawi Network of AIDS Service Organizations (MANASO) offices as the Community Linkage Groups (CLGs) implementing community led monitoring received bicycles to help them ease mobility challenges and fisher jackets for visibility.The items were requested by the CLGs after noting gaps which existed in the...
Chikwawa District Council Mainstreaming HIV and AIDS Interventions in Construction Development Projects.
Chikwawa District Council is proactively taking a leading role in mainstreaming HIV service provision to various sites where different construction development projects are taking place. The initiative focuses on promoting and optimizing the provision of HIV service uptake. The team is sensitizing the construction workers on the available HIV prevention options to prevent the spread...
NUHA CEESAY – OUTGOING UNAIDS MALAWI COUNTRY DIRECTOR BIDS FAREWELL TO STAKEHOLDERS IN THE HIV AND AIDS RESPONSE
The Joint United Nations Programme on HIV and AIDS (UNAIDS) Malawi Country Director, Nuha Ceesay is leaving Malawi for Eswatini after five years of successful mission in the country. Mr. Ceesay arrived and started his tour of duty in September 2019. He has been hailed by Stakeholders in the fight against HIV and AIDS for...
NAC PMRA SEND SHIVERS TO ADVERTISERS OF FAKE HIV CURE
On 10th July 2024, the National AIDS Commission (NAC) and the Pharmacy and Medicines Regulatory Authority (PMRA) issued a joint press statement, warning against the malpractice of advertising drugs purported to be cure for HIV without confirmation and permit from the two Government Institutions. Recent social media posts have seen numerous adverts of fake HIV...
JOINT STATEMENT ON INCREASING SPREAD OF FALSE SOCIAL MEDIA CLAIMS ABOUT HIV AND AIDS CURE
The National AIDS Commission (NAC) and the Pharmacy and Medicines Regulatory Authority (PMRA), pursuant to their mandates under the HIV and AIDS (Prevention and Management) Act No. 9 of 2018 and the PMRA Act No. 9 of 2019, respectively, have noted with concern increased spread of false, inaccurate and misleading information on HIV treatment, often...
KUCHULUKA KWA NCHITIDWE OFALITSA MAUTHENGA ABODZA OKHUDZA MANKHWALA A HIV NDI EDZI MMASAMBA A MCHEZO
Mabungwe a National AIDS Commission (NAC) ndi Pharmacy and Medicines Regulatory Authority (PMRA) adapatsidwa mphamvu ndi malamulo yowunika ndi kuvomereza mauthenga okhudza matenda a edzi komanso kuwonetsetsa kuti mankhwala achipatala, mankhwala a zitsamba ndi zakudya kapena zakumwa zimene zili mgulu la mankhwala ndi zabwino, zotetezeka ndi zogwira ntchito bwino, komanso kuti malamulo okhudza ntchito za...
NAC LEADING DISSEMINATION OF HIV & AIDS STRATEGIC DOCUMENTS
The National AIDS Commission (NAC) is disseminating key strategic documents and information on HIV and AIDS across the country. The exercise started in third week of June 2024 and is expected to end by 1st week of July 2024. Among the key strategic documents being disseminated are the 2024 HIV Estimates, the Revised National Strategic...
WOFALITSA ZABODZA ZOKHUDZANA MACHIRITSO A HIV AWERUZIDWA KUTI AKHALE M’NDENDE MIYEZI KHUMI NDI MPHAMBU ZISANU (15)
Bwalo la milandu laling’ono ku Mwanza lalamula a Petros Jasi kukakhala mu ndende chifukwa chonamiza anthu kuti ali ndi mankhwala omwe amachiza HIV dzina lake ‘Gamora wochiza HIV’. Masamba a Intaneti a mchezo adzadza ndi zonena za anthu ena omwe akumati ali ndi mankhwala omwe amachiza HIV omwe amatchedwa ‘Gamora wochiza HIV’. Anthuwa akhala akufalitsa...